LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 8/13 tsa. 3
  • Ndandanda ya Mlungu wa August 26

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa August 26
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
  • Tumitu
  • MLUNGU WA AUGUST 26
Utimiki Wathu wa Ufumu—2013
km 8/13 tsa. 3

Ndandanda ya Mlungu wa August 26

MLUNGU WA AUGUST 26

Nyimbo 63 ndi Pemphelo

□ Phunzilo la Baibo la Mpingo:

bt mutu 28 ndime 1 mpaka 7 (Mph. 30)

□ Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibo: Aroma 13 mpaka 16 (Mph. 10)

Kubweleza za M’sukulu ya Ulaliki (Mph. 20)

□ Msonkhano wa Nchito:

Nyimbo 11

Mph. 10: “Limbikitsani Kuyambitsa Maphunzilo a Baibo pa Ciŵelu Coyamba.” Nkhani. Pambuyo pake, mucite citsanzo ca mmene mungayambitsile phunzilo la Baibo pa Ciŵelu coyamba mu September. Limbikitsani onse kutengamo mbali.

Mph. 10: Njila Zolalikilila Uthenga Wabwino—Gawo la Mpingo Komanso Gawo Lanu-lanu. Nkhani yokambilana yocokela m’buku la Gulu, patsamba 102, ndime 3 mpaka tsamba 104, ndime 1. Funsani mafunso mtumiki wa magawo za makonzedwe a mpingo wanu okhalila ndi gawo logwililamo nchito.

Mph. 10: Cifukwa Cake Sindife Aneneli Onama. Nkhani yokambilana yocokela m’buku la Kukambitsilana, patsamba 35, ndime 3 mpaka kumapeto kwa tsamba 36.

Nyimbo 116 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani