LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 4/14 tsa. 8
  • Ndandanda ya Mlungu wa May 5

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa May 5
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Tumitu
  • MLUNGU WA MAY 5
Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
km 4/14 tsa. 8

Ndandanda ya Mlungu wa May 5

MLUNGU WA MAY 5

Nyimbo 33 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

jr mutu 8 ndime 1-7 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo Ekisodo 23-26 (Mph. 10 )

Na. 1: Ekisodo 25:1-22 (Mph. 4 kapena zocepelapo)

Na. 2: M’Baibulo Palibe Pamene Panalembedwa kuti Adamu Ankasunga Sabata —rs p. 346 ¶4–p. 347 ¶2 (Mph. 5)

Na. 3: Kodi Kukhulupilila Mizimu N’kutani? (bh tsa.100-103 ndime 10-13)

Msonkhano wa nchito:

Nyimbo 117

Mph. 10: Gaŵilani Magazini M’mwezi wa May. Kukambilana. Yambani ndi citsanzo coonetsa mmene mungagaŵilile magazini pogwilitsila nchito maulaliki aŵili acitsanzo amene ali patsamba lino. Ndiyeno kambilananinso maulaliki amenewa. Malizani mwa kulimbikitsa onse kuti azidziŵa bwino magazini iliyonse ndipo azigaŵila ena mosangalala.

Mph. 10: Zosoŵa za pa pampingo.

Mph. 10: Kodi tinacita zotani? Kukambilana. Pemphani omvela kuti afotokoze mapindu ndiponso zocitika za mu ulaliki zosangalatsa pa nkhani yakuti “Kuonjezela Luso Lathu mu Ulaliki—Kukhala Wofalitsa Wothandiza.”

Nyimbo 103 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani