LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 6/15 tsa. 7
  • Ndandanda ya Mlungu wa June 29

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Ndandanda ya Mlungu wa June 29
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Tumitu
  • MLUNGU WA JUNE 29
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 6/15 tsa. 7

Ndandanda ya Mlungu wa June 29

MLUNGU WA JUNE 29

Nyimbo 9 ndi Pemphelo

Phunzilo la Baibulo la Mpingo:

cl mutu 11 ndime 17-22 ndi bokosi pa tsa. 116 (Mph. 30)

Sukulu ya Ulaliki:

Kuŵelenga Baibulo: 1 Mafumu 3-6 (Mph. 8)

Kubweleza za m’Sukulu ya Ulaliki (Mph. 20)

Msonkhano wa Nchito:

Lemba la Mwezi: “Kumbukilani masiku akale.”—Deut. 32:7.

Nyimbo 118

Mph. 15: Zogaŵila mu July. Kukambilana. Kambilanani nkhani zimene zili mu zofalitsa zimene tidzagaŵila, ndipo mucite citsanzo coonetsa ofalitsa akuphunzitsa watsopano kugaŵila cofalitsa.

Mph. 15: Kalata Yocokela ku Bungwe Lolamulila. Kukambilana. Pemphani omvela kufotokoza mbali zolimbikitsa za lipoti la padziko lonse ndi za m’dziko lathu mu caka cautumiki capita.

Nyimbo 108 ndi Pemphelo

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani