LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • km 8/15 tsa. 4
  • Maulaliki Acitsanzo

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Maulaliki Acitsanzo
  • Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Nkhani Zofanana
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2014
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
  • Maulaliki Acitsanzo
    Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
Onaninso Zina
Utimiki Wathu wa Ufumu—2015
km 8/15 tsa. 4

Maulaliki Acitsanzo

Nsanja ya Mlonda July-August

“Mukanakhala ndi mphamvu zothetsa mavuto m’dzikoli, kodi mukanathetsa vuto liti? [Yembekezani yankho.] Baibulo limanena kuti posacedwapa, Mulungu adzathetsa vuto limeneli ndi ena ambili. [Ŵelengani lemba logwilizana ndi vuto limene wakamba, monga Danieli 2:44; Miyambo 2:21, 22; Mateyu 7:21-23 kapena 2 Petulo 3:7.] Magazini iyi ifotokoza nthawi imene Mulungu adzathetsa mavuto pa dziko lapansi ndi mmene adzawathetsela.”

Galamukani! September

“Tonse timadziŵa kuti ndalama n’zofunika pa umoyo wathu. Koma kodi muganiza kuti pangakhale ngozi iliyonse ngati munthu amakonda kwambili ndalama? [Yembekezani yankho.] Onani cenjezo limene Baibulo limapeleka. [Ŵelengani 1 Timoteyo 6:9.] Magazini iyi ifotokoza mmene tingakhalile ndi maganizo oyenela pa nkhani ya ndalama.”

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani