LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb19 November tsa. 2
  • Musamakonde Dziko Kapena Zinthu za M’dziko

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Musamakonde Dziko Kapena Zinthu za M’dziko
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
  • Nkhani Zofanana
  • Ganizilani Za Mtundu Wa Munthu Amene Muyenela Kukhala
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova—2013
  • Kanizani Ziyeso Mmene Yesu Anacitila
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2018
  • Zamkatimu
    Galamuka!—2022
  • M’kope Ino ya Galamuka!
    Galamuka!—2022
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2019
mwb19 November tsa. 2
M’bale akusankha zakumwa, akusankha zimene afuna kuona pa intaneti, komanso cipangizo ca m’manja cimene afuna kugula

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU | 1 YOHANE 1-5

Musamakonde Dziko Kapena Zinthu za M’dziko

2:15-17

Satana amaseŵenzetsa zinthu zitatu zotsatilazi, zimene ni zokopa za dzikoli, pofuna kuticotsa kwa Yehova. Kodi zinthu zimenezi mungazifotokoze bwanji kwa munthu wina?

  • “Cilakolako ca thupi”

  • “Cilakolako ca maso”

  • “Kudzionetsela ndi zimene munthu ali nazo pa moyo wake”

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani