LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 January tsa. 16
  • Thandizani Maphunzilo Anu a Baibo Kupewa Mayanjano Oipa

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Thandizani Maphunzilo Anu a Baibo Kupewa Mayanjano Oipa
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Thandizani Maphunzilo a Baibo Kuleka Makhalidwe Odetsa
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Thandizani Maphunzilo a Baibo Kukhala pa Ubale Wolimba na Yehova
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Thandizani Maphunzilo Anu a Baibo Kumapezeka pa Misonkhano
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Landilani Thandizo la Yehova Kupitila M’pemphelo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2021
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 January tsa. 16

CITANI KHAMA PA ULALIKI | WONJEZELANI CIMWEMWE CANU MU ULALIKI

Thandizani Maphunzilo Anu a Baibo Kupewa Mayanjano Oipa

Kuti ophunzila Baibo akhale pa ubwenzi na Yehova, ayenela kusankha mabwenzi abwino. (Sal. 15:1, 4) Mabwenzi abwino adzawalimbikitsa kucita zabwino.—Miy. 13:20; lff phunzilo 48.

Khalani acifundo pothandiza maphunzilo anu a Baibo kupewa mayanjano oipa. Zingakhale kuti zikuwavuta kuleka kugwilizana na mabwenzi a kudziko. Conco, muziwaonetsa cidwi ngakhale masiku amene simuphunzila nawo Baibo. Mungacite izi mwa kuwatumila meseji, foni, kapena kuwacezelako kwakanthawi. Pamene ophunzila Baibo anu akupita patsogolo, mungawaitanileko ku maceza amene anthu a Mulungu amakhala nawo nthawi zina. Mukatelo, adzaona kuti zimene akupeza n’zambili kuposa zimene akutaya. (Maliko 10:29, 30) Inunso mudzapeza cimwemwe poona kuti banja la Yehova likukula.

ONELELANI VIDIYO YAKUTI THANDIZANI MAPHUNZILO ANU A BAIBO KUPEWA MAYANJANO OIPA, KENAKO YANKHANI MAFUNSO AWA:

  • Kodi mayanjano oipa n’ciani?—1 Akor. 15:33

  • Kodi Rose anali kuganiza kuti maceza acikhristu amakhala otani?

  • Kodi Neeta anam’thandiza bwanji Rose kusiya mabwenzi oipa n’kupeza mabwenzi abwino?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani