LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 March tsa. 3
  • Kudzikweza Kumanyazitsa Munthu

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kudzikweza Kumanyazitsa Munthu
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Kumvela Kumaposa Nsembe
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Poyamba Sauli Anali Wodzicepetsa
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Mapulani a Davide a Kamenyedwe ka Nkhondo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • N’cifukwa Ciani Kudzicepetsa N’kofunikabe?
    Nsanja ya Mlonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yophunzila)—2017
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 March tsa. 3
Modzikweza, Sauli akupeleka nsembe yopseleza pa guwa la nsembe.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Kudzikweza Kumanyazitsa Munthu

Mfumu Sauli anaona kuti wathedwa nzelu (1 Sam. 13:​5-7)

M’malo motsatila malangizo a Yehova modzicepetsa, Sauli anacita zinthu modzikweza (1 Sam. 13:8,9; w00 8/1 13 ¶17)

Yehova anamulanga Sauli (1 Sam. 13:13, 14; w07 6/15 27 ¶8)

Kumakhala kudzikweza komanso kupanda nzelu ngati munthu afulumila kucita cinthu popanda cilolezo. Kudzikweza kumasiyana na kudzicepetsa. Ni zocitika monga ziti zimene zingapangitse munthu kudzikweza?

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani