LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb22 March tsa. 3
  • Kumvela Kumaposa Nsembe

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Kumvela Kumaposa Nsembe
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Nkhani Zofanana
  • Kudzikweza Kumanyazitsa Munthu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Mukhuthulileni za Mumtima Mwanu Yehova M’pemphelo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Kodi Mfumu Yanu N’ndani?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Mapulani a Davide a Kamenyedwe ka Nkhondo
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
mwb22 March tsa. 3
Mfumu Sauli watambasula dzanja, akuuza msilikali waciisiraeli amene wanyamula lupanga kuti asamuphe Agagi. Kumbuyo kwawo kuli msilikali wina amene akukusa gulu la nkhosa.

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Kumvela Kumaposa Nsembe

Mneneli wa Yehova anapatsa Mfumu Sauli malangizo omveka bwino (1 Sam. 15:3)

Sauli anayesa kudzilungamitsa atalephela kutsatila malangizo onse a Yehova (1 Sam. 15:13-15)

Yehova sakondwela na kulambila kwa anthu amene samumvela (1 Sam. 15:22, 23; w07 6/15 26 ¶4; it-2 521 ¶2)

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi nimamvela malangizo onse a gulu la Yehova mofulumila?’

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani