LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO
  • mwb23 January tsa. 3
  • Khalanibe Maso

Palibe vidiyo yake.

Pepani, vidiyo yakanga kulila.

  • Khalanibe Maso
  • Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Nkhani Zofanana
  • Kuleza Mtima kwa Yehova Kuli na Malile
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • Yehova Anapangitsa Zinthu Zosayembekezeleka Kucitika
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
  • N’cifukwa Ciyani Tiyenela Kukhala Odzicepetsa?
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
  • Nyamulani Mwana Wanu
    Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2022
Onaninso Zina
Umoyo na Utumiki Wathu Wacikhristu—Kabuku ka Misonkhano—2023
mwb23 January tsa. 3

CUMA COPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

Khalanibe Maso

Kwa zaka zambili, Yehova anali kucenjeza Ayuda kuti adzawakana ngati apitiliza kucita zoipa (2 Maf. 24:2, 3; w01 2/15 12 ¶2)

Iye anagwilitsa nchito Ababulo powononga Yerusalemu mu 607 B.C.E. (2 Maf. 25:8-10; w07 3/15 11 ¶10)

Yehova anapulumutsa anthu amene analabadila macenjezo ake (2 Maf. 25:11)

M’bale akulalikila mnzake ku nchito panthawi yopumula.

Kwa zaka zambili, iye wakhala akucenjeza anthu padzikoli kuti adzawononga “anthu osaopa Mulungu.”—2 Pet. 3:7.

DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi nimaseŵenzetsa mpata uliwonse umene napeza kuthandiza anthu kulabadila cenjezo la Mulungu?’—2 Tim. 4:2.

    Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
    Tulukani
    Loŵani
    • Cinyanja
    • Gawilani
    • Makonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenela Kutsatila
    • Mfundo Yosunga Cisinsi
    • Kusunga Cinsinsi
    • JW.ORG
    • Loŵani
    Gawilani