Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Esitere 8:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yesaya 14:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Yesaya 49:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Mafumu adzakhala okusamalira,+

      Ndipo ana awo aakazi adzakhala okuyamwitsira ana ako.

      Iwo adzakugwadira mpaka nkhope zawo pansi+

      Ndipo adzanyambita fumbi lakumapazi ako.+

      Choncho iwe udzadziwa kuti ine ndine Yehova.

      Anthu amene amandikhulupirira sadzachita manyazi.”+

  • Yesaya 60:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ana a anthu amene ankakupondereza adzabwera nʼkudzagwada pamaso pako.

      Anthu onse amene ankakuchitira zachipongwe adzagwada pamapazi ako,

      Ndipo adzakutchula kuti mzinda wa Yehova,

      Ziyoni wa Woyera wa Isiraeli.+

  • Yesaya 61:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 “Alendo adzabwera nʼkumaweta ziweto zanu,

      Ndipo anthu ochokera kwina+ adzakhala olima minda yanu ndi osamalira minda yanu ya mpesa.+

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani