Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • Misonkhano
  • Salimo 137:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Inu Yehova, kumbukirani

      Zimene Aedomu ananena pa tsiku limene Yerusalemu anawonongedwa.

      Iwo anati: “Gwetsani mzindawo! Ugwetseni mpaka pamaziko ake!”+

  • Yeremiya 49:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ponena za Edomu, Yehova wa magulu ankhondo akumwamba wanena kuti:

      “Kodi nzeru zinatha ku Temani?+

      Kodi anthu ozindikira sakuperekanso malangizo anzeru?

      Kodi nzeru zawo zinawola?

  • Yeremiya 49:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Taonani! Mofanana ndi chiwombankhanga mdani adzatsika nʼkugwira chakudya chake,+

      Ndipo adzatambasula mapiko ake pa Bozira.+

      Pa tsiku limenelo mtima wa asilikali a ku Edomu

      Udzakhala ngati mtima wa mkazi amene akubereka.”

Mabuku a Chinenero Chamanja cha ku Malawi (1993-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chinenero Chamanja cha ku Malawi
  • tumizirani
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • zachinsinsi
  • JW.ORG
  • Lowani
tumizirani