Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 13:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Mukutuluka lero m’mwezi wa Abibu.*+

  • Ekisodo 23:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Muzichita chikondwerero cha mikate yopanda chofufumitsa.+ Muzidya mikate yopanda chofufumitsa+ masiku 7 pa nthawi yake m’mwezi wa Abibu,*+ monga momwe ndakulamulirani, chifukwa munatuluka mu Iguputo m’mwezi umenewu. Ndipo palibe ayenera kuonekera kwa ine chimanjamanja.+

  • Ekisodo 34:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 “Muzisunga chikondwerero cha mkate wosafufumitsa.+ Monga momwe ndinakulamulirani, muzidya mkate wosafufumitsa masiku 7 m’mwezi wa Abibu*+ pa nthawi yoikidwiratu, chifukwa munatuluka mu Iguputo m’mwezi wa Abibu.

  • Numeri 28:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “‘M’mwezi woyamba, pa tsiku la 14, pazikhala pasika wa Yehova.+

  • Deuteronomo 16:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Muzisunga mwambo wa m’mwezi wa Abibu*+ pochita chikondwerero cha pasika kwa Yehova Mulungu wanu,+ chifukwa m’mwezi wa Abibu Yehova Mulungu wanu anakutulutsani mu Iguputo usiku.+

  • Esitere 3:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndiyeno m’mwezi woyamba,+ umene ndi mwezi wa Nisani,* m’chaka cha 12+ cha Mfumu Ahasiwero, munthu wina anachita Puri*+ kapena kuti Maere+ pamaso pa Hamani kuti adziwe tsiku ndi mwezi woyenerera. Choncho Maerewo anagwera mwezi wa 12 umene ndi mwezi wa Adara.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena