Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 11:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Sindingathe kuwasamalira ndekha anthuwa, chifukwa iwo ndi chimtolo chimene sindingathe kuchisenza.+

  • Deuteronomo 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Pa nthawi imeneyo ndinakuuzani kuti, ‘Ndekha sindikwanitsa kusenza mtolo wokutsogolerani.+

  • Machitidwe 6:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Chotero atumwi 12 aja anaitana khamu la ophunzira ndi kunena kuti: “N’kosayenera kuti ife tisiye ntchito yophunzitsa mawu a Mulungu n’kuyamba kugawa chakudya.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena