Numeri 13:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Iwo anabwera kwa Mose ndi Aroni, ndiponso kwa khamu lonse la ana a Isiraeli m’chipululu cha Parana, ku Kadesi.+ Anafotokozera onsewo za ulendo wawo n’kuwaonetsa zipatso za kudzikolo. Numeri 20:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Kenako khamu lonse la ana a Isiraeli linanyamuka ku Kadesi+ kuja n’kukafika kuphiri la Hora.+ Deuteronomo 1:46 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 46 Chotero munakhala ku Kadesi masiku ambiri.+ Deuteronomo 2:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Ndipo masiku amene tinayenda kuchokera ku Kadesi-barinea mpaka kuwoloka chigwa cha Zeredi anali zaka 38, kufikira m’badwo wa amuna otha kupita kunkhondo utatha pakati panu, monga mmene Yehova analumbirira kwa iwo.+ Oweruza 11:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Chifukwa Aisiraeli atatuluka mu Iguputo anayenda kudutsa m’chipululu kukafika ku Nyanja Yofiira+ mpaka ku Kadesi.+
26 Iwo anabwera kwa Mose ndi Aroni, ndiponso kwa khamu lonse la ana a Isiraeli m’chipululu cha Parana, ku Kadesi.+ Anafotokozera onsewo za ulendo wawo n’kuwaonetsa zipatso za kudzikolo.
14 Ndipo masiku amene tinayenda kuchokera ku Kadesi-barinea mpaka kuwoloka chigwa cha Zeredi anali zaka 38, kufikira m’badwo wa amuna otha kupita kunkhondo utatha pakati panu, monga mmene Yehova analumbirira kwa iwo.+
16 Chifukwa Aisiraeli atatuluka mu Iguputo anayenda kudutsa m’chipululu kukafika ku Nyanja Yofiira+ mpaka ku Kadesi.+