Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 30:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 “Ukamachita kalembera pa ana a Isiraeli, + aliyense wa iwo azipereka dipo la moyo wake kwa Yehova pa nthawi yowawerengayo,+ kuti mliri usawagwere pochita kalemberayo.+

  • Ekisodo 38:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Mwamuna aliyense amene anawerengedwa, kuyambira wa zaka 20 kupita m’tsogolo,+ anapereka hafu ya sekeli lolingana ndi hafu ya sekeli la kumalo oyera. Owerengedwa onse anakwana 603,550.+

  • Numeri 1:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Uwerenge+ khamu lonse la ana a Isiraeli malinga ndi mabanja awo, potsata nyumba za makolo awo, n’kulemba mayina awo. Uwerenge amuna onse, mmodzi ndi mmodzi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena