Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Choncho pa nthawi imeneyo tinatenga dzikoli kukhala lathu. Mafuko a Rubeni ndi Gadi+ ndinawapatsa Aroweli,+ mzinda umene uli m’chigwa cha Arinoni, ndi hafu ya dera lamapiri la Giliyadi, ndi mizinda yake.

  • Yoswa 1:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndipo Yehova akadzapereka mpumulo kwa abale anu, monga waperekera kwa inu, nawonso abale anu akakalanda dziko limene Yehova Mulungu akuwapatsa,+ m’pamene inuyo mudzabwerere. Mudzabwerera kudziko la cholowa chanu limene Mose mtumiki wa Yehova wakugawirani,+ tsidya lino la Yorodano, kum’mawa kuno.’”+

  • Yoswa 13:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Mose mtumiki wa Yehova anapereka cholowa kwa hafu ina ya fuko la Manase, kwa Arubeni ndi kwa Agadi, kutsidya la kum’mawa kwa Yorodano.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena