Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 1:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Atatero, anasonkhanitsa anthu onse pa tsiku loyamba la mwezi wachiwiri. Anawasonkhanitsa n’cholinga chakuti awalembe m’kaundula+ kuti adziwe mibadwo yawo malinga ndi mabanja awo, ndiponso nyumba za makolo awo. Anawalemba mayina kuyambira azaka 20 kupita m’tsogolo,+ mmodzi ndi mmodzi.

  • Deuteronomo 29:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “Nonsenu mwaima pano lero pamaso pa Yehova Mulungu wanu, inu atsogoleri a mafuko, akulu anu, atsogoleri anu, mwamuna aliyense wa mu Isiraeli,+

  • Yeremiya 4:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Nenani zimenezi mu Yuda anthu inu, ndipo zilengezeni ngakhale mu Yerusalemu.+ Fuulani ndi kuliza lipenga la nyanga ya nkhosa m’dziko lonse.+ Fuulani kuti: “Sonkhanani pamodzi, ndipo tiyeni tilowe m’mizinda yokhala ndi mipanda yolimba kwambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena