17 “Posamutsa chihema chokumanako,+ gulu la msasa wa Alevi+ lizikhala pakati pa magulu a misasa ina.
“Dongosolo limene azilitsatira posamuka,+ n’limenenso azitsatira pomanga misasa yawo, aliyense m’malo ake, malinga ndi chigawo chawo cha mafuko atatu.