Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 2:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 “Posamutsa chihema chokumanako,+ gulu la msasa wa Alevi+ lizikhala pakati pa magulu a misasa ina.

      “Dongosolo limene azilitsatira posamuka,+ n’limenenso azitsatira pomanga misasa yawo, aliyense m’malo ake, malinga ndi chigawo chawo cha mafuko atatu.

  • Numeri 3:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Mabanja a Agerisoni anali kukhala kumbuyo kwa chihema chopatulika.+ Anali kumanga msasa wawo kumadzulo.

  • Numeri 3:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Mabanja a ana a Kohati anali kumanga msasa wawo kum’mwera kwa chihema chopatulika.+

  • Numeri 3:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Mtsogoleri wa nyumba ya mabanja a Merari anali Zuriyeli, mwana wa Abihaili. Iwo anali kumanga msasa wawo kumpoto kwa chihema chopatulika.+

  • Numeri 3:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Amene anali kumanga msasa wawo kum’mawa kwa chihema chopatulika, kumbali yotulukira dzuwa, anali Mose ndi Aroni, ndiponso ana a Aroni. Ntchito yawo inali kutumikira m’malo opatulika,+ kutumikira ana a Isiraeli. Aliyense amene si Mlevi akayandikira malowo, anayenera kuphedwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena