Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 40:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kuti ndipezeke kuno anachita chondiba kudziko la Aheberi,+ ndiponso kuno palibe chilichonse chimene ndinalakwa choti andiikire m’ndende muno.”+

  • Ekisodo 21:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Wakuba munthu+ ndi kum’gulitsa+ kapena munthu amene wapezeka ndi munthu wobedwayo, aziphedwa ndithu.+

  • 1 Timoteyo 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 adama,+ amuna ogonana ndi amuna anzawo, oba anthu, onama, olumbira monama,+ ndiponso ochita china chilichonse chosagwirizana+ ndi chiphunzitso cholondola.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena