Deuteronomo 20:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 chifukwa Yehova Mulungu wanu akuyenda limodzi nanu kuti akumenyereni nkhondo ndi kukupulumutsani kwa adani anu.’+ Yoswa 10:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Palibe tsiku lina lofanana ndi limenelo, kaya pambuyo pake kapena patsogolo pake, loti Yehova anamvera mawu a munthu mwa njira imeneyi,+ popeza Yehova mwiniyo anali kumenyera nkhondo Isiraeli.+ Yoswa 10:42 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 42 Yoswa anagwira mafumu onsewa n’kulanda malo awo pa nthawi imodzi,+ chifukwa Yehova Mulungu wa Isiraeli ndiye anali kuwamenyera nkhondo.+ Salimo 44:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Pakuti iwo sanatenge dzikolo chifukwa cha lupanga lawo,+Ndipo si mkono wawo umene unawabweretsera chipulumutso.+Koma chinabwera ndi dzanja lanu lamanja,+ mkono wanu ndi kuwala kwa nkhope yanu,Chifukwa munakondwera nawo.+
4 chifukwa Yehova Mulungu wanu akuyenda limodzi nanu kuti akumenyereni nkhondo ndi kukupulumutsani kwa adani anu.’+
14 Palibe tsiku lina lofanana ndi limenelo, kaya pambuyo pake kapena patsogolo pake, loti Yehova anamvera mawu a munthu mwa njira imeneyi,+ popeza Yehova mwiniyo anali kumenyera nkhondo Isiraeli.+
42 Yoswa anagwira mafumu onsewa n’kulanda malo awo pa nthawi imodzi,+ chifukwa Yehova Mulungu wa Isiraeli ndiye anali kuwamenyera nkhondo.+
3 Pakuti iwo sanatenge dzikolo chifukwa cha lupanga lawo,+Ndipo si mkono wawo umene unawabweretsera chipulumutso.+Koma chinabwera ndi dzanja lanu lamanja,+ mkono wanu ndi kuwala kwa nkhope yanu,Chifukwa munakondwera nawo.+