Genesis 16:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Pamenepo Sarai mkazi wa Abulamu anapereka Hagara, kapolo wake Mwiguputo, kwa mwamuna wake Abulamu kuti akhale mkazi wake.+ Zimenezi zinachitika Abulamu atakhala zaka 10 m’dziko la Kanani. Ekisodo 21:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Ngati mbuye wake sanakondwere naye kuti akhale mkazi wake wamng’ono+ koma wamulola kuwomboledwa, mbuyeyo alibe ufulu womugulitsa kwa anthu a mtundu wina chifukwa wam’chitira zachinyengo. 2 Samueli 5:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Pambuyo pake, Davide anatenganso adzakazi+ ndi akazi+ ena mu Yerusalemu atachoka ku Heburoni, moti anaberekanso ana ena aamuna ndi aakazi. 2 Mbiri 11:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Rehobowamu anali kukonda kwambiri Maaka mdzukulu wa Abisalomu kuposa akazi ake ena onse+ ndi adzakazi* ake, pakuti iye anakwatira akazi 18, ndiponso anali ndi adzakazi 60. Iye anabereka ana aamuna 28 ndi ana aakazi 60.
3 Pamenepo Sarai mkazi wa Abulamu anapereka Hagara, kapolo wake Mwiguputo, kwa mwamuna wake Abulamu kuti akhale mkazi wake.+ Zimenezi zinachitika Abulamu atakhala zaka 10 m’dziko la Kanani.
8 Ngati mbuye wake sanakondwere naye kuti akhale mkazi wake wamng’ono+ koma wamulola kuwomboledwa, mbuyeyo alibe ufulu womugulitsa kwa anthu a mtundu wina chifukwa wam’chitira zachinyengo.
13 Pambuyo pake, Davide anatenganso adzakazi+ ndi akazi+ ena mu Yerusalemu atachoka ku Heburoni, moti anaberekanso ana ena aamuna ndi aakazi.
21 Rehobowamu anali kukonda kwambiri Maaka mdzukulu wa Abisalomu kuposa akazi ake ena onse+ ndi adzakazi* ake, pakuti iye anakwatira akazi 18, ndiponso anali ndi adzakazi 60. Iye anabereka ana aamuna 28 ndi ana aakazi 60.