Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 15:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ahiti,+ Aperezi,+ Arefai,+

  • Ekisodo 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Choncho nditsikira kwa iwo kuti ndiwalanditse m’manja mwa Aiguputo,+ ndi kuwatulutsa m’dzikolo, n’kuwalowetsa m’dziko labwino komanso lalikulu, dziko loyenda mkaka ndi uchi.+ Ndiwalowetsa m’dziko la Akanani, Ahiti, Aamori, Aperizi, Ahivi, ndi Ayebusi.+

  • Yoswa 9:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mafumu+ a kutsidya kwa Yorodano anamva zimene zinachitika. Amenewa anali mafumu a Ahiti,+ Aamori, Akanani,+ Aperezi,+ Ahivi ndi Ayebusi.+ Iwo anali kukhala kudera lamapiri, ndiponso ku Sefela, ndi m’mbali monse mwa Nyanja Yaikulu,+ komanso pafupi ndi Lebanoni.+ Mafumu onsewo atangomva zimene zinachitikazo,

  • Oweruza 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ana a Isiraeli anakhala pakati pa Akanani,+ amene ndi Ahiti, Aamori, Aperezi, Ahivi ndi Ayebusi.+

  • 1 Mafumu 9:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Anthu onse otsala a Aamori,+ Ahiti,+ Aperezi,+ Ahivi,+ ndi Ayebusi,+ amene sanali ana a Isiraeli,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena