Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 18:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kumadzulo kwa gawolo, malirewo anakhotera kum’mwera, paphiri loyang’anizana ndi kum’mwera kwa Beti-horoni. Kuchokera pamenepo anakathera ku Kiriyati-baala, kutanthauza Kiriyati-yearimu,+ womwe ndi mzinda wa ana a Yuda. Awa ndiwo malire a kumadzulo a gawo la Benjamini.

  • Oweruza 18:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Amunawa ananyamuka pa ulendo wawo ndipo anayenda mpaka kukafika pafupi ndi Kiriyati-yearimu+ ku Yuda, n’kumanga msasa pamenepo. N’chifukwa chake malowo amatchedwa dzina lakuti Mahane-dani*+ kufikira lero. Malo amenewa ali kumadzulo kwa Kiriyati-yearimu.

  • 1 Mbiri 13:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Chotero, Davide anasonkhanitsa+ Aisiraeli onse kuchokera kumtsinje wa Iguputo+ mpaka kukafika polowera ku Hamati,+ kuti akatenge likasa+ la Mulungu woona ku Kiriyati-yearimu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena