Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 18:47
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 47 Mulungu woona ndiye Wobwezera adani anga.+

      Iye amagonjetsa mitundu ya anthu ndi kuiika kunsi kwa mapazi anga.+

  • Salimo 110:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 110 Yehova wauza Ambuye wanga kuti:+

      “Khala kudzanja langa lamanja+

      Kufikira nditaika adani ako monga chopondapo mapazi ako.”+

  • Salimo 144:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Iye amandisonyeza kukoma mtima kwake kosatha ndipo ndiye malo anga achitetezo,+

      Malo anga okwezeka ndi Wopereka chipulumutso,+

      Chishango+ changa ndi malo anga othawirako.+

      Iye amandigonjetsera mitundu ya anthu.+

  • 1 Akorinto 15:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Pakuti ayenera kulamulira monga mfumu kufikira Mulungu ataika adani onse pansi pa mapazi+ ake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena