Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 11:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Kenako Davide anatuma nthumwi kuti akamutenge.+ Choncho mkaziyo anabweradi kwa Davide+ ndipo Davide anagona naye+ pa nthawi imene mkaziyo anali kudziyeretsa ku chodetsa chake.+ Zitatero mkaziyo anabwerera kunyumba yake.

  • 2 Samueli 11:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Pamapeto pake, Davide anauza Uriya kuti: “Pita kunyumba kwako ukasambe mapazi ako.”+ Uriya anatuluka m’nyumba ya mfumu ndipo pambuyo pake mfumuyo inamutumizira mphatso.

  • 2 Samueli 11:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kuwonjezera apo, Davide anamuitana kuti adye ndi kumwa naye pamodzi, ndipo anamuledzeretsa.+ Ngakhale zinali choncho, madzulo Uriya anapita kwa atumiki a mbuye wake kukagona pabedi, ndipo sanapite kunyumba kwake.

  • 2 Samueli 11:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 M’kalatamo analembamo kuti:+ “Muike Uriya kutsogolo kumene nkhondo yakula,+ ndipo inu mubwerere m’mbuyo kuti amukanthe ndipo afe ndithu.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena