-
2 Mafumu 3:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Kuwonjezera apo, inatumiza uthenga kwa Yehosafati mfumu ya Yuda, wakuti: “Mfumu ya Mowabu yandipandukira. Kodi upita nane kukamenya nkhondo ku Mowabu?” Yehosafati anayankha kuti: “Inde ndipita.+ Iwe ndi ine ndife amodzi. Anthu ako ndi anthu anga ndi amodzi.+ Mahatchi anga n’chimodzimodzi ndi mahatchi ako.”
-