Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 92:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Anthu oipa akamaphuka ngati msipu,+

      Ndipo anthu onse ochita zopweteka anzawo akamaphuka ngati maluwa,

      Amatero kuti awonongeke kwamuyaya.+

  • Yesaya 40:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Udzu wobiriwirawo wauma ndipo maluwawo afota+ chifukwa mpweya wa Yehova wauzirapo.+ Ndithu anthu ali ngati udzu wobiriwira.+

  • Yakobo 1:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Dzuwa limatuluka ndi kutentha kwake n’kufotetsa zomera, ndipo maluwa a zomerazo amathothoka. Kukongola kwake kumatha. Momwemonso munthu wachuma adzafa akutsatira njira ya moyo wake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena