2 Mafumu 5:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Koma Elisa anatuma mthenga kukamuuza kuti: “Pita ukasambe+ maulendo 7+ mumtsinje wa Yorodano, kuti mnofu wako ubwerere mwakale ndi kuti iweyo+ ukhale woyera.” 2 Mbiri 20:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Anthuwo ananyamuka m’mawa kwambiri n’kupita kuchipululu+ cha Tekowa.+ Ali m’njira, Yehosafati anaimirira n’kunena kuti: “Tamverani inu Ayuda ndi anthu okhala mu Yerusalemu!+ Khulupirirani+ Yehova Mulungu wanu kuti mukhalitse. Khulupirirani aneneri+ ake kuti zinthu zikuyendereni bwino.” 1 Petulo 5:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Chimodzimodzinso inu anyamata. Muzigonjera+ amuna achikulire. Koma nonsenu muzichitirana zinthu modzichepetsa,+ chifukwa Mulungu amatsutsa odzikweza, koma odzichepetsa amawasonyeza kukoma mtima kwake kwakukulu.+
10 Koma Elisa anatuma mthenga kukamuuza kuti: “Pita ukasambe+ maulendo 7+ mumtsinje wa Yorodano, kuti mnofu wako ubwerere mwakale ndi kuti iweyo+ ukhale woyera.”
20 Anthuwo ananyamuka m’mawa kwambiri n’kupita kuchipululu+ cha Tekowa.+ Ali m’njira, Yehosafati anaimirira n’kunena kuti: “Tamverani inu Ayuda ndi anthu okhala mu Yerusalemu!+ Khulupirirani+ Yehova Mulungu wanu kuti mukhalitse. Khulupirirani aneneri+ ake kuti zinthu zikuyendereni bwino.”
5 Chimodzimodzinso inu anyamata. Muzigonjera+ amuna achikulire. Koma nonsenu muzichitirana zinthu modzichepetsa,+ chifukwa Mulungu amatsutsa odzikweza, koma odzichepetsa amawasonyeza kukoma mtima kwake kwakukulu.+