Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 14:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Choncho Yowabu anatumiza anthu ku Tekowa+ kuti akatenge mkazi wanzeru.+ Atabwera naye, Yowabu anamuuza kuti: “Chonde ukhale ngati munthu amene ali panyengo yolira maliro, ndipo uvale zovala za panyengo yolira maliro, komanso usadzole mafuta.+ Ukatero ukhale ngati mkazi amene wakhala akulira maliro kwa masiku ambiri.+

  • 1 Mbiri 4:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ashari+ bambo wa Tekowa+ anali ndi akazi awiri, Hela ndi Naara.

  • 2 Mbiri 11:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Anamanganso mizinda ya Betelehemu,+ Etami,+ Tekowa,+

  • Yeremiya 6:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Bisalani, inu ana a Benjamini, thawani pakati pa Yerusalemu. Ku Tekowa+ imbani lipenga la nyanga ya nkhosa.+ Ku Beti-hakeremu+ kwezani moto wa chizindikiro, chifukwa chiwonongeko chachikulu, tsoka, lasuzumira kuchokera kumpoto.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena