Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 15:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 M’chaka chachiwiri cha Peka mwana wa Remaliya mfumu ya Isiraeli, Yotamu+ mwana wa Uziya+ mfumu ya Yuda anakhala mfumu.

  • 1 Mbiri 3:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Yehoasi anabereka Amaziya,+ Amaziya anabereka Azariya,+ Azariya anabereka Yotamu,+

  • 2 Mbiri 26:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Mfumu Uziya+ inakhalabe yakhate mpaka tsiku limene inamwalira. Iyo inali kungokhala m’nyumba ina chifukwa cha khatelo+ osagwiranso ntchito, popeza inali itachotsedwa m’nyumba ya Yehova. Pa nthawiyi, Yotamu mwana wake ndiye anali kuyang’anira nyumba ya mfumu ndi kuweruza anthu a m’dzikolo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena