Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 22:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Koma Mikaya anati: “Pali Yehova Mulungu wamoyo,+ zimene Yehova anene kwa ine n’zimene ndikalankhule.”+

  • Yeremiya 23:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Mneneri amene walota maloto anene maloto akewo. Koma amene ndamuuza mawu anga, alankhule mawu angawo moona.”+

      “Kodi mapesi a tirigu angafanane ndi tirigu weniweniyo?”+ watero Yehova.

  • Yeremiya 42:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Pamenepo mneneri Yeremiya anawayankha kuti: “Ndamva zimene mwanenazo. Ndipemphera kwa Yehova Mulungu wanu malinga ndi zimene mwapempha.+ Ndipo mawu aliwonse amene Yehova angakuyankheni ndidzakuuzani.+ Sindidzakubisirani kalikonse.”+

  • Machitidwe 20:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Pakuti sindinakubisireni kanthu, koma ndinakuuzani chifuniro+ chonse cha Mulungu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena