Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 10:37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 37 Komanso tinafunika kupititsa ufa woyambirira wamisere,+ zopereka zathu,+ zipatso za mtengo uliwonse,+ vinyo watsopano+ ndi mafuta+ kwa ansembe kumalo odyera+ m’nyumba ya Mulungu wathu. Tinafunikanso kupititsa chakhumi kwa Alevi+ pa zinthu zochokera m’nthaka yathu, pakuti Aleviwo anali kulandira chakhumi kuchokera m’mizinda yathu yonse ya zaulimi.

  • Nehemiya 12:47
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 47 Aisiraeli onse m’masiku a Zerubabele+ komanso m’masiku a Nehemiya+ anali kupereka gawo loyenera kwa oimba+ ndi alonda a pachipata+ malinga ndi zofunikira zawo za tsiku ndi tsiku. Ndipo anali kupatula gawolo ndi kulipereka kwa Alevi.+ Aleviwo anali kupatula gawolo ndi kulipereka kwa ana a Aroni.

  • Malaki 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Kodi munthu wochokera kufumbi angabere Mulungu? Komatu inu mukundibera.”

      Inu mukunena kuti: “Takuberani motani?”

      “Mukundibera kudzera m’chakhumi* ndi m’zopereka.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena