Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yohane 11:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Pamenepo Yesu anati: “Ine ndine kuuka ndi moyo.+ Aliyense wokhulupirira mwa ine, ngakhale amwalire, adzakhalanso ndi moyo.+

  • Machitidwe 26:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “N’chifukwa chiyani anthu inu mukuona ngati n’zosatheka kuti Mulungu aukitse akufa?+

  • 1 Akorinto 15:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Tsopano ngati timalalikira kuti Khristu anaukitsidwa kwa akufa,+ bwanji ena mwa inu akunena kuti akufa sadzaukitsidwa?+

  • Chivumbulutso 20:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Nyanja inapereka akufa amene anali mmenemo. Nayonso imfa ndi Manda zinapereka akufa+ amene anali mmenemo. Aliyense wa iwo anaweruzidwa malinga ndi ntchito zake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena