Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 28:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Udzakhala wotembereredwa mumzinda,+ udzakhala wotembereredwa m’munda.+

  • Yobu 21:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kodi nyale ya oipa imazimitsidwa kangati?+

      Ndipo tsoka lawo limawagwera kangati?

      Kodi ndi kangati pamene Mulungu amawakwiyira ndi kuwalanga?+

  • Miyambo 3:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Temberero la Yehova lili panyumba ya munthu woipa,+ koma malo okhala anthu olungama, iye amawadalitsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena