Salimo 58:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Wolungama adzasangalala chifukwa chakuti waona oipa akupatsidwa chilango.+Adzasambitsa mapazi ake m’magazi a anthu oipa.+ Yesaya 37:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 awa ndi mawu otsutsana naye amene Yehova wanena:“Namwali, mwana wamkazi wa Ziyoni, wakunyoza ndipo wakuseka.+Kumbuyo kwako, mwana wamkazi wa Yerusalemu wakupukusira mutu.+ Chivumbulutso 18:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 “Kondwerani kumwambako+ chifukwa cha zimene zamuchitikira. Inunso oyera,+ inu atumwi,+ ndi inu aneneri, kondwerani chifukwa Mulungu wamuweruza ndi kumupatsa chilango chifukwa cha zomwe anakuchitirani.”+
10 Wolungama adzasangalala chifukwa chakuti waona oipa akupatsidwa chilango.+Adzasambitsa mapazi ake m’magazi a anthu oipa.+
22 awa ndi mawu otsutsana naye amene Yehova wanena:“Namwali, mwana wamkazi wa Ziyoni, wakunyoza ndipo wakuseka.+Kumbuyo kwako, mwana wamkazi wa Yerusalemu wakupukusira mutu.+
20 “Kondwerani kumwambako+ chifukwa cha zimene zamuchitikira. Inunso oyera,+ inu atumwi,+ ndi inu aneneri, kondwerani chifukwa Mulungu wamuweruza ndi kumupatsa chilango chifukwa cha zomwe anakuchitirani.”+