-
Yesaya 51:6Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
6 “Kwezani maso anu kumwamba,+ ndipo yang’anani padziko lapansi. Pakuti kumwamba kudzabenthukabenthuka n’kumwazidwa ngati utsi,+ ndipo dziko lapansi lidzatha ngati chovala.+ Anthu okhalamo adzafa ngati ntchentche. Koma chipulumutso changa chidzakhala mpaka kalekale+ ndipo chilungamo changa sichidzaphwanyika.+
-
-
Danieli 9:24Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
24 “Pali milungu 70 imene yaikidwa yokhudza anthu a mtundu wako+ ndi mzinda wanu woyera,+ ndi cholinga choti athetse kuphwanya malamulo,+ athetse machimo,+ aphimbe cholakwa,+ abweretse chilungamo kuti chikhalepo mpaka kalekale,+ adinde chidindo+ pa masomphenya ndi maulosi, ndiponso kuti adzoze Malo Opatulikitsa.+
-