Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 36:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Inu Mulungu, chilungamo chanu chili ngati mapiri anu.+

      Chiweruzo chanu ndi chozama kwambiri ngati madzi akuya.+

      Inu Yehova, mumapulumutsa munthu ndiponso nyama.+

  • Yesaya 51:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “Kwezani maso anu kumwamba,+ ndipo yang’anani padziko lapansi. Pakuti kumwamba kudzabenthukabenthuka n’kumwazidwa ngati utsi,+ ndipo dziko lapansi lidzatha ngati chovala.+ Anthu okhalamo adzafa ngati ntchentche. Koma chipulumutso changa chidzakhala mpaka kalekale+ ndipo chilungamo changa sichidzaphwanyika.+

  • Danieli 9:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 “Pali milungu 70 imene yaikidwa yokhudza anthu a mtundu wako+ ndi mzinda wanu woyera,+ ndi cholinga choti athetse kuphwanya malamulo,+ athetse machimo,+ aphimbe cholakwa,+ abweretse chilungamo kuti chikhalepo mpaka kalekale,+ adinde chidindo+ pa masomphenya ndi maulosi, ndiponso kuti adzoze Malo Opatulikitsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena