Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 7:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Tsopano inu Yehova Ambuye Wamkulu Koposa, ndinu Mulungu woona. Kunena za mawu anu, akhale oona,+ pakuti mwandilonjeza ine mtumiki wanu zabwino zimenezi.+

  • 1 Mafumu 17:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Mayiyo ataona zimenezi anauza Eliya kuti: “Tsopano ndadziwadi kuti ndinu munthu wa Mulungu+ ndipo mawu a Yehova amene ali m’kamwa mwanu ndi oona.”+

  • Salimo 12:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Mawu a Yehova ndi oyengeka bwino,+

      Ngati siliva woyengedwa nthawi zokwanira 7 mung’anjo ya m’nthaka.

  • Salimo 119:140
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 140 Mawu anu ndi oyengeka kwambiri,+

      Ndipo ine mtumiki wanu ndimawakonda.+

  • Miyambo 30:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mawu alionse a Mulungu ndi oyera.+ Iye ndi chishango kwa onse othawira kwa iye.+

  • Yohane 17:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ayeretseni+ ndi choonadi. Mawu+ anu ndiwo choonadi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena