Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 28:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Golide woyenga bwino sangaperekedwe mosinthana nazo,+

      Ndipo sangayeze siliva monga mtengo wake.

  • Miyambo 8:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Landirani malangizo* anga osati siliva, ndiponso kudziwa zinthu m’malo mwa golide wabwino kwambiri.+

  • Miyambo 16:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Kupeza nzeru n’kwabwino kwambiri kuposa kupeza golide.+ Ndipo ndi bwino kusankha kumvetsa zinthu kuposa siliva.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena