Salimo 97:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Inu okonda Yehova+ danani nacho choipa.+Iye amateteza moyo wa anthu ake okhulupirika.+Amawalanditsa m’manja mwa anthu oipa.+ Salimo 101:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Sindidzaika maso anga pa chinthu chilichonse chopanda pake.+Ndimadana ndi zochita za opatuka pa choonadi.+Sindilola kuti zochita zawozo zindikhudze.+ Miyambo 13:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Wolungama amadana ndi lilime lonama,+ koma anthu oipa amachita zinthu zochititsa manyazi ndipo amadzibweretsera manyazi.+ Miyambo 16:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Cholakwa chimaphimbika ndi kukoma mtima kosatha ndiponso choonadi,+ ndipo chifukwa choopa Yehova munthu amapatuka pa choipa.+ Aroma 12:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Chikondi+ chanu chisakhale cha chiphamaso.+ Nyansidwani ndi choipa,+ gwiritsitsani chabwino.+
10 Inu okonda Yehova+ danani nacho choipa.+Iye amateteza moyo wa anthu ake okhulupirika.+Amawalanditsa m’manja mwa anthu oipa.+
3 Sindidzaika maso anga pa chinthu chilichonse chopanda pake.+Ndimadana ndi zochita za opatuka pa choonadi.+Sindilola kuti zochita zawozo zindikhudze.+
5 Wolungama amadana ndi lilime lonama,+ koma anthu oipa amachita zinthu zochititsa manyazi ndipo amadzibweretsera manyazi.+
6 Cholakwa chimaphimbika ndi kukoma mtima kosatha ndiponso choonadi,+ ndipo chifukwa choopa Yehova munthu amapatuka pa choipa.+