Yobu 17:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Chonde, mundisungire chotsimikizira changa.+Palinso ndani amene angagwirane nane chanza+ monga chikole? Miyambo 6:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Mwana wanga, ngati walonjeza kuti udzapereka ngongole ya mnzako iye akadzalephera kubweza,+ ngati wagwirana chanza ndi mlendo pochita mgwirizano,+ Miyambo 11:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Munthu amene walonjeza kuti adzapereka ngongole ya mlendo iye akadzalephera kubweza,+ zinthu sizidzamuyendera bwino. Koma wodana ndi kugwirana chanza pochita mgwirizano sakhala ndi nkhawa. Miyambo 22:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Usakhale pakati pa anthu ogwirana chanza,+ pakati pa anthu amene amakhala chikole cha ngongole za anthu ena.+
3 Chonde, mundisungire chotsimikizira changa.+Palinso ndani amene angagwirane nane chanza+ monga chikole?
6 Mwana wanga, ngati walonjeza kuti udzapereka ngongole ya mnzako iye akadzalephera kubweza,+ ngati wagwirana chanza ndi mlendo pochita mgwirizano,+
15 Munthu amene walonjeza kuti adzapereka ngongole ya mlendo iye akadzalephera kubweza,+ zinthu sizidzamuyendera bwino. Koma wodana ndi kugwirana chanza pochita mgwirizano sakhala ndi nkhawa.
26 Usakhale pakati pa anthu ogwirana chanza,+ pakati pa anthu amene amakhala chikole cha ngongole za anthu ena.+