Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 28:66
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 66 Pamenepo moyo wako udzakhala pangozi yaikulu koopsa, ndipo udzakhala wamantha usiku ndi usana, moti sudzakhala wotsimikiza za moyo wako.+

  • 2 Mafumu 19:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Anthu okhala m’mizindayo adzafooka manja.+

      Adzachita mantha kwambiri ndiponso adzachita manyazi.+

      Adzakhala ngati zomera zakutchire, ndi udzu wanthete wobiriwira,+

      Ngati udzu womera padenga+ ukawauka ndi mphepo yotentha yakum’mawa.+

  • Salimo 48:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Iwo anaona ndipo anadabwa.

      Anasokonezeka, moti anathawa mopanikizika kwambiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena