Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 102:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Masiku a moyo wanga ali ngati chithunzithunzi chimene chimazimiririka dzuwa likalowa,+

      Ndipo ndauma ngati udzu.+

  • Yesaya 37:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Anthu okhala m’mizindayo adzafooka manja.+

      Adzachita mantha kwambiri ndiponso adzachita manyazi.+

      Adzakhala ngati zomera zakutchire, ndi udzu wanthete wobiriwira,+

      Ngati udzu womera padenga+ ndiponso wa m’mizere ya m’munda, ukawauka ndi mphepo yotentha yakum’mawa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena