Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 9:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma Ambuye anamuuza kuti: “Nyamuka uzipita, chifukwa munthu ameneyu ndi chiwiya changa chochita kusankhidwa+ chotengera dzina langa kupita nalo kwa anthu a mitundu ina,+ komanso kwa mafumu+ ndi ana a Isiraeli.

  • Machitidwe 10:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Iwo anati: “Tachokera kwa Koneliyo, kapitawo wa asilikali. Iye ndi munthu wolungama ndi woopa Mulungu,+ amene mtundu wonse wa Ayuda umamuyamikira.+ Mngelo woyera anamupatsa malangizo a Mulungu kuti atume anthu kudzakutengani kuti mupite kunyumba kwake, akamve zimene inu mukanene.”

  • Aroma 10:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Koma Yesaya analankhula molimba mtima kwambiri kuti: “Anthu amene anandipeza ndi amene sanali kundifunafuna.+ Ndinaonekera kwa anthu amene sanafunse za ine kuti andipeze.”+

  • Aroma 15:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 koma ndichite monga mmene Malemba amanenera kuti: “Amene chilengezo chonena za iye sichinawapeze adzaona, ndipo amene sanamve adzazindikira.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena