Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 31:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Nditabwerera kwa inu ndinadzimvera chisoni.+ Mutandithandiza kuzindikira ndinadzimenya pantchafu chifukwa cha chisoni.+ Ndinachita manyazi ndipo ndinanyazitsidwa+ chifukwa cha chitonzo cha paubwana wanga.’”+

  • Ezekieli 16:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 M’zonyansa zako zonse ndi m’zochita zako zauhule sunakumbukire masiku a ubwana wako pamene unali wosavala ndi wamaliseche, pamene unali kuponyaponya timiyendo tako m’mwamba uli m’magazi ako.+

  • Ezekieli 16:60
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 60 Ndithu ine ndidzakumbukira pangano limene ndinapangana ndi iwe m’masiku a ubwana wako,+ ndipo ndidzakukhazikitsira pangano limene lidzakhalepo mpaka kalekale.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena