Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 36:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Amadya ndi kukhuta chakudya chonona m’nyumba mwanu.+

      Ndipo mumawamwetsa mumtsinje wa zosangalatsa zanu zambiri.+

  • Salimo 63:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Moyo wanga wakhutira ndi gawo labwino kwambiri, wakhutira ndi zinthu zabwino kwambiri,+

      Ndipo milomo yanga ikukutamandani ndi mfuu yachisangalalo.+

  • Mateyu 22:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Kenako inatumanso akapolo ena+ kuti, ‘Kauzeni oitanidwawo kuti: “Ine ndakonza chakudya chamasana,+ ng’ombe zanga komanso nyama zanga zonenepa zaphedwa, ndipo zinthu zonse zakonzedwa kale. Bwerani ku phwando laukwati.”’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena