Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 29:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Liwu la Yehova lili pamwamba pa madzi,*+

      Liwu la Mulungu waulemerero+ lagunda ngati bingu.+

      Yehova ali pamwamba pa madzi ambiri.+

  • Salimo 65:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Iye akutontholetsa phokoso la nyanja,+

      Akutontholetsa phokoso la mafunde ake komanso chipwirikiti cha mitundu ya anthu.+

  • Chivumbulutso 16:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mngelo wachiwiri+ anathira mbale yake m’nyanja.+ Ndipo nyanja inasanduka magazi+ ngati a munthu wakufa, moti chamoyo chilichonse m’nyanjamo chinafa.+

  • Chivumbulutso 17:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mmodzi wa angelo 7 amene anali ndi mbale 7+ aja, anabwera n’kundiuza kuti: “Bwera, ndikuonetsa chiweruzo cha hule lalikulu+ lokhala pamadzi ambiri,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena