Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 67:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Dziko lapansi lidzapereka zipatso zake.+

      Mulungu, ndithu Mulungu wathu, adzatidalitsa.+

  • Salimo 115:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Yehova watikumbukira, ndipo adzapereka madalitso,+

      Adzadalitsa nyumba ya Isiraeli,+

      Adzadalitsa nyumba ya Aroni.+

  • Yesaya 61:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ana awo adzadziwika pakati pa mitundu ya anthu,+ ndipo mbadwa zawo zidzadziwika pakati pa anthu osiyanasiyana. Onse owaona adzazindikira+ kuti iwo ndi ana odalitsidwa ndi Yehova.”+

  • Yesaya 65:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Yehova wanena kuti: “Monga momwe vinyo watsopano+ amapezekera m’tsango la mphesa ndipo wina amanena kuti, ‘Musaliwononge,+ pakuti muli dalitso mmenemu,’+ inenso ndidzachita zomwezo chifukwa cha atumiki anga, kuti ndisawawononge onse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena