Levitiko 26:32 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 32 Dziko lanu ndidzalisandutsa bwinja,+ ndipo adani anu amene adzakhala m’dzikolo adzaliyang’anitsitsa modabwa.+ Yeremiya 10:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Tamvetserani nkhani imene yamveka! Kugunda kwakukulu kukumveka kuchokera kudziko la kumpoto,+ ndipo kudzasandutsa mizinda ya Yuda kukhala mabwinja, malo obisalamo mimbulu.+ Yeremiya 12:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Cholowa changacho achisandutsa bwinja+ moti chafota ndipo chawonongeka.+ Dziko lonse lakhala bwinja ndipo palibe aliyense amene zikumukhudza.+ Ezekieli 11:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Nditangomaliza kulosera, Pelatiya mwana wa Benaya anamwalira.+ Choncho ine ndinagwada n’kuwerama mpaka nkhope yanga pansi, n’kufuula+ kuti: “Kalanga ine, inu Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa!+ Kodi mukufuna kufafaniziratu Aisiraeli otsalawa?”+
32 Dziko lanu ndidzalisandutsa bwinja,+ ndipo adani anu amene adzakhala m’dzikolo adzaliyang’anitsitsa modabwa.+
22 Tamvetserani nkhani imene yamveka! Kugunda kwakukulu kukumveka kuchokera kudziko la kumpoto,+ ndipo kudzasandutsa mizinda ya Yuda kukhala mabwinja, malo obisalamo mimbulu.+
11 Cholowa changacho achisandutsa bwinja+ moti chafota ndipo chawonongeka.+ Dziko lonse lakhala bwinja ndipo palibe aliyense amene zikumukhudza.+
13 Nditangomaliza kulosera, Pelatiya mwana wa Benaya anamwalira.+ Choncho ine ndinagwada n’kuwerama mpaka nkhope yanga pansi, n’kufuula+ kuti: “Kalanga ine, inu Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa!+ Kodi mukufuna kufafaniziratu Aisiraeli otsalawa?”+