Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 32:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndileke tsopano kuti mkwiyo wanga uwayakire ndipo ndiwafafanize,+ koma iwe ndikupange kukhala mtundu waukulu.”+

  • Yeremiya 11:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “Tsopano iwe, usawapempherere anthu awa, ndipo usawalirire kwa ine mochonderera. Usawaperekere pemphero,+ chifukwa ine sindidzamvetsera pamene iwo akundiitana chifukwa cha tsoka limene lawagwera.+

  • Yeremiya 14:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Yehova anapitiriza kundiuza kuti: “Usapempherere anthu awa kuti zinthu ziwayendere bwino.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena