Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 37:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Amuna inu mvetserani mwatcheru kugunda kwa mawu a Mulungu,+

      Ndi kubangula kochokera m’kamwa mwake.

  • Yobu 38:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Kodi ungafuulire mtambo

      Kuti madzi ochuluka akukhuthukire?+

  • Yobu 38:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Ndani anaika nzeru+ m’mitambo,

      Kapena zinthu zochitika kuthambo, ndani anazipatsa kuzindikira?+

  • Salimo 18:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ali kumwamba, Yehova anayamba kugunda ngati mabingu,+

      Wam’mwambamwamba anayamba kutulutsa mawu ake,+

      Anatulutsanso matalala ndi makala onyeka a moto.

  • Salimo 68:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Imbirani Iye wokwera kumwamba kwa kumwamba kwakale.+

      Tamverani! Iye akulankhula ndi mawu amphamvu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena